17. Pakuti amadya cakudya ca ucimo,Namwa vinyo wa cifwamba.
18. Koma mayendedwe a olungama akunga kuunika kwa mbanda kuca,Kunkabe kuwala kufikira usana woti mbe.
19. Njira ya oipa ikunga mdima;Sadziwa cimene ciwapunthwitsa,
20. Mwananga, tamvera mau anga;Cherera makutu ku zonena zanga.