Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Miyambi 31:3-7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Musapereke mphamvu yako kwa akazi,Ngakhale kuyenda m'njira yoononga mafumu.

4. Mafumu, Lemueli, mafumu sayenera kumwa vinyo;Akalonga sayenera kunena, Cakumwa caukali ciri kuti?

5. Kuti angamwe, naiwale malamulo,Naweruze mokhota anthu onse osautsidwa.

6. Wofuna kufa umpatse cakumwa caukali,Ndi vinyo kwa owawa mtima;

7. Amwe, narwale umphawi wace, Osakumbukiranso bvuto lace.

Werengani mutu wathunthu Miyambi 31