21. Saopera banja lace cipale cofewa;Pakuti banja lace lonse libvala mlangali.
22. Adzipangira zimbwi zamaangamaanga;Nabvala bafuta ndi guta woti biriwiri.
23. Mwamuna wace adziwika kubwalo,Pokhala pakati pa akuru a dziko.
24. Asoka maraya abafuta, nawagulitsa;Napereka mipango kwa wogulitsa malonda.