2. Ciani mwananga, Ciani mwana wa mimba yanga?Ciani mwana wa zowinda zanga?
3. Musapereke mphamvu yako kwa akazi,Ngakhale kuyenda m'njira yoononga mafumu.
4. Mafumu, Lemueli, mafumu sayenera kumwa vinyo;Akalonga sayenera kunena, Cakumwa caukali ciri kuti?
5. Kuti angamwe, naiwale malamulo,Naweruze mokhota anthu onse osautsidwa.
6. Wofuna kufa umpatse cakumwa caukali,Ndi vinyo kwa owawa mtima;