6. M'kulakwa kwa woipa muli msampha;Koma wolungama ayimba, nakondwera.
7. Wolungama asamalira mlandu wa osauka;Koma woipa alibe nzeru yakuudziwa.
8. Anthu onyoza atentha mudzi;Koma anzeru alezetsa mkwiyo.
9. Munthu wanzeru akatsutsana ndi munthu wopusa,Ngakhale akwiya, ngakhale aseka, palibe mtendere.