Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Miyambi 27:22-27 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

22. Ungakhaleukonolacitsirum'mtondo ndi munsi, pamodzi ndi mphale,Koma utsiru wace sudzamcoka.

23. Udziwitsitse zoweta zako ziri bwanji,Samalira magulu ako;

24. Pakuti cuma siciri cosatha;Kodi korona alipobe mpaka mibadwo mibadwo?

25. Amatuta maudzu, msipu uoneka,Achera masamba a kumapiri,

26. Ana a nkhosa akubveka,Atonde aombolera munda;

27. Mkaka wa mbuzi udzakukwanira kudya;Ndi a pa banja lako ndi adzakazi ako.

Werengani mutu wathunthu Miyambi 27