14. Monga citseko cikankhikira pa zitsulo za pamphuthu,Momwemo wolesi agubuduka pakama pace.
15. Wolesi alonga dzanja lace m'mbale;Kumtopetsa kulibweza kukamwa kwace.
16. Wolesi adziyesa wanzeruKoposa anthu asanu ndi awiri akuyankha mozindikira.
17. Wakungopita ndi kubvutika ndi ndeu yosakhala yaceAkunga wogwira makutu a garu.
18. Monga woyaruka woponya nsakali,Mibvi, ndi imfa,