Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Miyambi 24:5-10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

5. Mwamuna wanzeru ngwamphamvu;Munthu wodziwa ankabe nalimba.

6. Pakuti udzaponya nkhondo yako ndi upo,Ndi kupulumuka pocuruka aphungu,

7. Nzeru itarikira citsiru;Satsegula pakamwa kubwalo.

8. Wolingalira zakucita zoipaAnthu adzamcha waciwembu.

9. Maganizo opusa ndiwo cimo;Wonyoza anyansa anthu.

10. Ukalefuka tsiku la tsokaMphamvu yako icepa.

Werengani mutu wathunthu Miyambi 24