28. Munthu wokhota amautsa makani;Kazitape afetsa ubwenzi.
29. Munthu waciwawa akopa mnzace,Namuyendetsa m'njira yosakhala bwino.
30. Wotsinzina ndiye aganizira zakhota;Wosunama afikitsa zoipa.
31. Imvi ndiyo korona wa ulemu,Idzapezedwa m'njira ya cilungamo.
32. Wosakwiya msanga aposa wamphamvu;Wolamulira mtima wace naposa wolanda mudzi.
33. Maere aponyedwa pamfunga;Koma ndiye Yehova alongosola zonse.