18. Kunyada kutsogolera kuonongekaMtinia wodzikuza ndi kutsogolera kupunthwa.
19. Kufatsa mtima ndi osaukaKuposa kugawana zofunkha ndi onyada.
20. Wolabadira mau adzapeza bwino;Ndipo wokhulupirira Yehova adala.
21. Wanzeru mtima adzachedwa wocenjera;Ndipo kukoma kwa milomo kuyenjezera kuphunzira.