1. Malongosoledwe a mtima nga munthu;Koma mayankhidwe a lilime acokera kwa Yehova.
2. Njira zonse za munthu ziyera pamaso pace;Koma Yehova ayesa mizimu.
3. Pereka zocita zako kwa Yehova,Ndipo zolingalira zako zidzakhazikika.
4. Zonse Yehova anazipangaziri ndi zifukwa zao;Ngakhale amphulupulu kuti aone tsiku loipa,