12. Udani upikisanitsa;Koma cikondi cikwirira zolakwa zonse.
13. Nzeru ipezedwa m'milomo ya wozindikira;Koma wopusa pamsana pace ntyole.
14. Anzeru akundika zomwe adziwaKoma m'kamwa mwa citsiru muononga tsopano lino.
15. Cuma ca wolemera ndi mudzi wace wolimba;Koma umphawi wao uononga osauka.