Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mika 6:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Anthu anga, kumbukilanitu cofunsira Balaki mfumu ya Moabu, ndi comuyankha Balamu mwana wa Beori, kuyambira ku Sitimu kufikira ku Giligala; kuti mudziwe zolungama za Yehova.

Werengani mutu wathunthu Mika 6

Onani Mika 6:5 nkhani