Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mika 5:2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma iwe, Betelehemu Efrata, ndiwe wamng'ono kuti ukhale mwa zikwi za Yuda, mwa iwe mudzanditurukira wina wakudzakhala woweruza m'Israyeli; maturukiro ace ndiwo a kale lomwe, kuyambira nthawi yosayamba.

Werengani mutu wathunthu Mika 5

Onani Mika 5:2 nkhani