Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Mika 4:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nyamuka nupunthe, mwana wamkazi wa Ziyoni; pakuti ndidzasanduliza nyanga yako ikhale yacitsulo, ndi ziboda zako zikhale zamkuwa; ndipo udzaphwanya mitundu yambiri ya anthu; ndipo uzipereka ciperekere phindu lao kwa Yehova, ndi cuma cao kwa Ambuye wa dziko lonse lapansi.

Werengani mutu wathunthu Mika 4

Onani Mika 4:13 nkhani