Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 89:49-52 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

49. Ciri kuti cifundo canu cakale, Ambuye,Munacilumbirira Davide pa cikhulupiriko canu?

50. Kumbukilani, Ambuye, cotonzera atumiki anu;Ndicisenza m'cifuwa mwanga cacokera ku mitundu yonse yaikuru ya anthu;

51. Cimene adani anu, Yehova, atonza naco;Cimene atonzera naco mayendedwe a wodzozedwa wanu.

52. Wodalitsika Yehova ku nthawi yonse,Amen ndi Amen.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 89