Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 89:35-39 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

35. Ndinalumbira kamodzi m'ciyero canga;Sindidzanamizira Davide;

36. Mbeu yace idzakhala ku nthawi yonse,Ndi mpando wacifumu wace ngati dzuwa pamaso panga.

37. Udzakhazikika ngati mwezi ku nthawi yonse,Ndi ngati mboni yokhulupirika kuthambo.

38. Koma Inu munamtaya, nimunamkaniza,Munakwiya naye wodzozedwa wanu.

39. Munakaniza cipangano ca mtumiki wanu;Munaipsa korona wace ndi kumponya pansi,

Werengani mutu wathunthu Masalmo 89