Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 89:23-25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

23. Ndipo ndidzaphwanya omsautsa pamaso pace;Ndidzapandanso odana naye.

24. Koma cikhulupiriko canga ndi cifundo canga zidzakhala naye;Ndipo nyanga yace idzakwezeka m'dzina langa.

25. Ndipo ndidzaika dzanja lace panyanja,Ndi dzanja lamanja lace pamitsinje.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 89