16. Mundibwerere ine, ndi kundicitira cifundo;Mpatseni mtumiki wanu mphamvu yanu,Ndipo pulumutsani mwana wa mdzakazi wanu.
17. Mundicitire cizindikilo coti cabwino;Kuti ondida acione, nacite manyazi,Popeza Inu, Yehova, munandithandiza ndi kundisangalatsa,