Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 85:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndidzamva colankhula Mulungu Yehova;Pakuti adzalankhula zamtendere ndi anthu ace, ndi okondedwa ace;Koma asabwererenso kucita zapusa.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 85

Onani Masalmo 85:8 nkhani