Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 84:4-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

4. Odala iwo akugonera m'nyumba mwanu;Akulemekezani cilemekezere,

5. Wodala munthu amene mphamvu yace iri mwa Inu;Mumtima mwace muli makwalala a ku Ziyoni,

6. Popyola cigwa ca kulira misozi aciyesa ca akasupe;Inde mvula: ya cizimalupsa icidzaza ndi madalitso.

7. Apita mwamphamvu naonjezapo mphamvu,Aoneka pamaso pa Mulungu m'Ziyoni.

8. Yehova Mulungu wa makamu, imvani pemphero langa:Cherani khutu, Mulungu wa Yakobo.

9. Onani, Mulungu, ndinu cikopa cathu;Ndipo penyani pa nkhope ya Wodzozedwa wanu.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 84