Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 80:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Mbusa wa Israyeli, cherani khutu;Inu wakutsogolera Yosefe ngati nkhosa;Inu wokhala pa akerubi, walitsani.

2. Utsani camuna canu pamaso pa Efraimu ndi Benjamini ndi Manase,Ndipo mutidzere kutipulumutsa.

3. Mutibweze, Mulungu;Nimuwalitse nkhope yanu, ndipo tidzapulumuka.

4. Yehova, Mulungu wa makamu,Mudzakwiyira pemphero la anthu anu kufikira liti?

Werengani mutu wathunthu Masalmo 80