8. Pakuti m'dzanja la Yehova muli cikho;Ndi vinyo wace acita thobvu;Cidzala ndi zosanganizira, ndipo atsanulako:Indedi, oipa onse a pa dziko lapansi adzamwaNadzagugudiza nsenga zace.
9. Koma ine ndidzalalikira kosalekeza,Ndidzayimbira zomlemekeza Mulungu wa Yakobo.
10. Ndipo ndidzatseteka nyanga zonse za oipa;Koma nyanga za wolungama zidzakwezeka.