Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 74:13-18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

13. Mudagawa nyanja ndi mphamvu yanu;Mudaswa mitu ya zoopsa za m'madzi.

14. Mudaphwanya mitu ya livyatanu;Mudampereka akhale cakudya ca iwo a m'cipululu.

15. Mudagawa kasupe ndi mtsinje;Mudaphwetsa mitsinje yaikuru.

16. Usana ndi wanu, usikunso ndi wanu:Munakonza kuunika ndi dzuwa.

17. Munaika malekezero onse a dziko lapansi;Munalenga dzinja ndi malimwe.

18. Mukumbukile ici, Yehova, mdaniyo anatonza,Ndipo anthu opusa ananyoza dzina lanu.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 74