Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 73:26-28 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

26. Likatha thupi langa ndi mtima wanga:Mulungu ndiye thanthwe la mtima wanga, ndi colandira canga cosatha.

27. Pakuti, taonani, iwo okhala patali ndi Inu adzaonongeka;Muononga onse akupembedza kwina, kosiyana ndi Inu.

28. Koma ine, kundikomera kuyandikiza kwa Mulungu:Ndimuyesa Ambuye Yehova pathawirapo ine,Kuti ndifotokozere nchito zanu zonse,

Werengani mutu wathunthu Masalmo 73