14. Taonani, ali m'cikuta ca zopanda pace;Anaima ndi cobvuta, nabala bodza.
15. Anacita dzenje, nalikumba,Nagwa m'mbuna yomwe anaikumba.
16. Cobvuta cace cidzambwerera mwini,Ndi ciwawa cace cidzamgwera pakati pamutu pace.
17. Ndidzayamika Yehova monga mwa cilungamo cace;Ndipo ndidzayimbira Yehova Wam'mwambamwamba.