Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 69:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipulumutseni Mulungu;Pakuti madzi afikira moyo wanga.

2. Ndamira m'thope lozama, lopanda poponderapo;Ndalowa m'madzi ozama, ndipo cigumula candimiza.

3. Ndalema ndi kupfuula kwanga; kum'mero kwauma gwa:M'maso mwanga mwada poyembekeza Mulungu wanga.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 69