Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 65:1-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. M'Ziyoni akulemekezani Inu mwacete, Mulungu:Adzakucitirani Inu cowindaci.

2. Wakumva pemphero Inu,Zamoyo zonse zidzadza kwa Inu.

3. Mphulupulu zinandilaka;Koma mudzafafaniza zolakwa zathu.

4. Wodala munthuyo mumsankha, ndi kumyandikizitsa,Akhale m'mabwalo anu:Tidzakhuta nazo zokoma za m'nyumba yanu,Za m'malo oyera a Kacisi wanu.

5. Mudzatiyankha nazo zoopsa m'cilungamo,Mulungu wa cipulumutso cathu;Ndinu cikhulupiriko ca malekezero Onse a dziko lapansi,Ndi ca iwo okhala kutali kunyanja:

Werengani mutu wathunthu Masalmo 65