5. Mudzakhutitsa moyo wanga ngati ndi mafuta ndi zonona;Ndipo pakamwa panga ndidzakulemekezani ndi milomo yakupfuula mokondwera;
6. Pokumbukira Inu pa kama wanga,Ndi kulingalira za Inu maulonda a usiku.
7. Pakuti munakhala mthandizi wanga;Ndipo ndidzapfuula mokondwera mu mthunzi wa mapiko anu.
8. Moyo wanga uumirira Inu:Dzanja lamanja lanu lindigwiriziza.