Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 63:5-8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

5. Mudzakhutitsa moyo wanga ngati ndi mafuta ndi zonona;Ndipo pakamwa panga ndidzakulemekezani ndi milomo yakupfuula mokondwera;

6. Pokumbukira Inu pa kama wanga,Ndi kulingalira za Inu maulonda a usiku.

7. Pakuti munakhala mthandizi wanga;Ndipo ndidzapfuula mokondwera mu mthunzi wa mapiko anu.

8. Moyo wanga uumirira Inu:Dzanja lamanja lanu lindigwiriziza.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 63