4. Koma mwapatsa mbendera akuopa Inu,Aikweze cifukwa ca coonadi.
5. Kuti okondedwa anu alanditsidwe,Pulumutsani ndi dzanja lanu lamanja, ndipo mutibvomereze.
6. Mulungu walankhula m'ciyero cace; ndidzakondwerera:Ndidzagawa Sekemu, ndidzayesa muyeso cigwa ca Sukoti.