Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 56:5-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

5. Tsiku lonse atenderuza mau anga:Zolingirira zao zonse ziri pa ine kundicitira coipa.

6. Amemezana, alalira,Achereza mapazi anga,Popeza alindira moyo wanga.

7. Kodi adzapulumuka ndi zopanda pace?Gwetsani anthu mumkwiyo, Mulungu.

8. Muwerenga kuthawathawa kwanga:Sungani misozi yanga m'nsupa yanu;Kodi siikhala m'buku mwanu?

9. Pamenepo adani anga adzabwerera m'mbuyo tsiku lakuitana ine:Ici ndidziwa, kuti Mulungu abvomerezana nane.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 56