Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 55:16-20 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

16. Koma ine ndidzapfuulira kwa Mulungu;Ndipo Yehova atizandipulumutsa.

17. Madzulo, m'mawa, ndi msana ndidzadandaula, ndi kubuula,Ndipo adzamva mau anga.

18. Anaombola moyo wanga ku nkhondo yondilaka, ndikhale mumtendere:Pakuti ndiwo ambiri okangana nane.

19. Mulungu adzamva, nadzawasautsa,Ndiye wokhalabe ciyambire kale lomwe.Popeza iwowa sasinthika konse,Ndipo saopa Mulungu.

20. Anaturutsa manja ace awagwire iwo akuyanjana naye:Anaipsa pangano lace.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 55