Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 36:3-6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

3. Mau a pakamwa pace ndiwo opanda pace ndi onyenga:Waleka kuzindikira ndi kucita bwino.

4. Alingirira zopanda pace pakama pace;Adziika panjira posad pabwino;Coipa saipidwa naco.

5. Yehova, m'mwambamuli cifundo canu;Coonadi canu cifikira kuthambo.

6. Cilungamo canu cikunga mapiri a Mulungu;Maweruzo anu akunga cozama cacikuru:Yehova, musunga munthu ndi nyama.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 36