1. Colakwa ca woipayo cimati m'kati mwa mtima wanga,Palibe kuopa Mulungu pamaso pace.
2. Pakud adzidyoletsa yekha m'kuona kwace,Kuti anthu sadzacipeza coipa cace ndi kukwiya naco.
3. Mau a pakamwa pace ndiwo opanda pace ndi onyenga:Waleka kuzindikira ndi kucita bwino.