Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 24:7-10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

7. Weramutsani mitu yanu, zipata inu;Ndipo kwezekani inu, zitseko zosatha:Kuti Mfumu ya ulemerero ilowe.

8. Mfumu imene ya ulemerero ndani?Yehova wamphamvu ndi wolimba,Yehova wolimba kunkhondo.

9. Weramutsani mitu yanu, zipata inu;Inde weramutsani, zitseko zosatha inu,Kuti Mfumu ya ulemerero ilowe.

10. Mfumu imene ya ulemerero ndani?Yehova wa makamu makamu, Ndiye Mfumu ya ulemerero.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 24