7. Weramutsani mitu yanu, zipata inu;Ndipo kwezekani inu, zitseko zosatha:Kuti Mfumu ya ulemerero ilowe.
8. Mfumu imene ya ulemerero ndani?Yehova wamphamvu ndi wolimba,Yehova wolimba kunkhondo.
9. Weramutsani mitu yanu, zipata inu;Inde weramutsani, zitseko zosatha inu,Kuti Mfumu ya ulemerero ilowe.
10. Mfumu imene ya ulemerero ndani?Yehova wa makamu makamu, Ndiye Mfumu ya ulemerero.