Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 21:7-10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

7. Pakuti mfumu akhulupirira Yehova,Ndipo mwa cifundo ca Wam'mwambamwamba sadzagwedezeka iye,

8. Dzanja lanu lidzapeza adani anu onse:Dzanja lanu lamanja lidzapeza iwo akuda Inu.

9. Mudzawaika ngati ng'anjo yamoto pa nyengo ya mkwiyo wanu.Yehova adzawatha m'kukwiya kwace,Ndipo moto udzawanyeketsa.

10. Mudzaziononga zobala zao kuzicotsa pa dziko lapansi,Ndi mbeu zao mwa ana a anthu.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 21