10. Tsono, mafumu inu, citani mwanzeru:Langikani, oweruza inu a dziko lapansi.
11. Tumikirani Yehova ndi mantha,Ndipo kondwerani ndi cinthenthe.
12. Mpsompsoneni Mwanayo, kuti angakwiye, ndipo mungatayike m'njira,Ukayaka pang'ono pokha mkwiyo wace.Odala onse akumkhulupirira Iye.