Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 17:6-9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

6. Ine ndinakuitanani, pakuti mudzandiyankha, Mulungu:Cherani khutu lanu kwa ine, imvani mau anga.

7. Onetsani cifundo canu codabwiza, Inu wakupulumutsa okhulupirira InuKwa iwo akuwaukira ndi dzanja lanu lamanja.

8. Ndisungeni monga kamwana ka m'diso,Ndifungatireni mu mthunzi wa mapiko anu,

9. Kundilanditsa kwa oipa amene andipasula,Adani a pa moyo wanga amene andizinga.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 17