Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 17:3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Mwayesera mtima wanga; mwandizonda usiku;Mwandisuntha, simupeza kanthu;Ndatsimikiza mtima kuti m'kamwa mwanga simudzalakwa.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 17

Onani Masalmo 17:3 nkhani