Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 145:18-21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

18. Yehova ali pafupi ndi onse akuitanira kwa Iye,Onse akuitanira kwa Iye m'coonadi.

19. Adzacita cokhumba iwo akumuopa;Nadzamva kupfuula kwao, nadzawapulumutsa.

20. Yehova asunga onse akukondana naye;Koma oipa onse adzawaononga.

21. Pakamwa panga padzanena cilemekezo ca Yehova;Ndi zinthu zonse zilemekeze dzina lace loyera ku nthawi za nthawi.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 145