Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 145:15-19 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

15. Maso a onse ayembekeza Inu;Ndipo muwapatsa cakudya cao m'nyengo zao.

16. Muniowetsa dzanja lanu,Nimukwaniritsira zamoyo zonse cokhumba cao.

17. Yehova ali wolungama m'njira zace zonse,Ndi wacifundo m'nchito zace zonse.

18. Yehova ali pafupi ndi onse akuitanira kwa Iye,Onse akuitanira kwa Iye m'coonadi.

19. Adzacita cokhumba iwo akumuopa;Nadzamva kupfuula kwao, nadzawapulumutsa.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 145