1. Yehova, ndaitana kwa Inu; ndifulumireni ine;Mundicherere khutu, pamene ndiitana kwa Inu.
2. Pempherolanga liikike ngaticofukiza pamaso panu;Kukweza manja anga kuikike ngati nsembe ya madzulo.
3. Muike mdindo pakamwa panga, Yehova;Sungani pakhomo pa milomo yanga.