Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 127:1-3 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Akapanda kumanga nyumba Yehova,Akuimanga agwiritsa nchito cabe;Akapanda kusunga mudzi Yehoya,Mlonda adikira cabe.

2. Kuli cabe kwa inu Rulawirira mamawa ndi kusagonerapo madzulo,Kudya mkate wosautsa kuupeza;Kuli tero kuti izi apatsa okondedwa ace ngati m'tulo.

3. Taonani ana ndiwo colandira ca kwa Yehova;Cipatso ca m'mimba ndico mphotho yace.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 127