Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 122:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndinakondwera m'mene ananena nane,Tiyeni ku nyumba ya Yehova.

2. Mapazi athu alinkuima M'zipata zanu, Yerusalemu.

3. Yerusalemu anamangidwaNgati mudzi woundana bwino:

4. Kumene akwerako mafuko, ndiwo mafuko a Yehova;Akhale mboni ya kwa Israyeli,Ayamike dzina la Yehova.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 122