1. Ndinakondwera m'mene ananena nane,Tiyeni ku nyumba ya Yehova.
2. Mapazi athu alinkuima M'zipata zanu, Yerusalemu.
3. Yerusalemu anamangidwaNgati mudzi woundana bwino:
4. Kumene akwerako mafuko, ndiwo mafuko a Yehova;Akhale mboni ya kwa Israyeli,Ayamike dzina la Yehova.