Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 121:2-6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

2. Thandizo langa lidzera kwa Yehova,Wakulenga zakumwamba ndi dziko lapansi.

3. Sadzalola phazi lako literereke:Iye amene akusunga sadzaodzera.

4. Taonani, wakusunga IsrayeaSadzaodzera kapena kugona.

5. Yehova ndiye wakukusunga;Yehova ndiye mthunzi wako wa ku dzanja lako lamanja.

6. Dzuwa silidzawamba usana,Mwezi sudzakupanda usiku.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 121