Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 120:4-7 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

4. Mibvi yakuthwa ya ciphona.Ndi makara tsanya.

5. Tsoka ine, kuti ndiri mlendo m'Meseke,Kuti ndigonera m'mahema a Kedara!

6. Moyo wanga unakhalitsa nthawiPamodzi ndi iye wakudana nao mtendere.

7. Ine ndikuti, Mtendere;Koma polankhula ine, iwowa akuti, Nkhondo.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 120