Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 119:86-90 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

86. Malamulo anu onse ngokhulupirika;Andilondola nalo bodza; ndithandizeni.

87. Akadandithera pa dziko lapansi; Koma ine sindinasiya malangizo anu.

88. Mundipatse moyo monga mwa cifundo canu;Ndipo ndidzasamalira mboni ya pakamwa panu,

89. Mau anu aikika kumwamba,Kosatha, Yehova.

90. Cikhulupiriko canu cifikira mibadwo mibadwo;Munakhazikitsa dziko lapansi, ndipo likhalitsa.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 119