51. Odzikuza anandinyoza kwambiri:Koma sindinapatukanso naco cilamulo canu.
52. Ndinakumbukila maweruzo anu kuyambira kale, Yehova,Ndipo ndinadzitonthoza.
53. Ndinasumwa kwakukuru,Cifukwa ca oipa akusiya cilamulo canu.
54. Malemba anu anakhala nyimbo zangaM'nyumba ya ulendo wanga,