Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 119:172-176 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

172. Lilime langa liyimbire mau anu;Pakuti malamulo anu onse ndiwo olungama.

173. Dzanja lanu likhale lakundithandizaPopezandinasankha malangizo anu.

174. Ndinakhumba cipulumutso canu, Yehova;Ndipo cilamulo canu ndico condikondweretsa.

175. Mzimu wanga ukhale ndi moyo, ndipo udzakulemekezani;Ndipo maweruzo anu andithandize.

176. Ndinasocera ngati nkhosa yotayika; funani mtumiki wanu;Pakuti sindiiwala malamulo anu.

Werengani mutu wathunthu Masalmo 119