Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Masalmo 119:120-124 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

120. Thupi langa linjenjemera ndi kuopa Inu;Ndipo ndicita mantha nao maweruzo anu.

121. Ndinacita ciweruzo ndi cilungamo;Musandisiyira akundisautsa.

122. Mumkhalire cikole mtumiki wanucimkomere;Odzikuza asandisautse.

123. Maso anga anatha mphamvu pafuna cipulumutso canu,Ndi mau a cilungamo canu.

124. Mucitire mtumiki wanu monga mwa cifundo canu,Ndipo ndiphunzitseni malemba anu,

Werengani mutu wathunthu Masalmo 119